Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/09 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 2
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 2
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 10/09 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa November 2

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 2

Nyimbo Na. 115

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 28, ndime 14 mpaka 21, ndi bokosi patsamba 289

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 14-18

Na. 1: Deuteronomo 15:1-15

Na. 2: Kodi Kuopa Mulungu Kumaphatikizapo Chiyani?

Na. 3: Mulungu Anakumbukira Mwana Wake (lr-CN mutu 39)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 1

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kuyambitsa Maphunziro a Baibulo. Kukambirana ndi omvera. Sankhani ofalitsa angapo ndipo apempheni kuti afotokoze zimene zinachitika pamene amayambitsa maphunziro pa tsiku limene linasankhidwa kuchita ntchito yapadera imeneyi. Lengezani tsiku lotsatira limene lasankhidwa kudzayambitsa maphunziro a Baibulo, ndipo chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zosonyeza mmene tingayambitsire maphunziro a Baibulo.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Kulalikira M’kalata. Nkhani yokambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 71 mpaka tsamba 73.

Nyimbo Na. 9

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena