Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/10 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 1

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 1
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 1
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 2/10 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa March 1

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 1

Nyimbo Na. 20

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 4 ndime 1-11

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Rute 1-4

Na. 1: Rute 3:1-13

Na. 2: Mmene Kukhala Achifundo Kumatipindulitsira (Mat. 5:7)

Na. 3: Kodi Chilango cha Uchimo N’chiyani? (rs tsa.149 ndime 2 mpaka 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 42

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kuyambitsa Maphunziro a Baibulo. Lengezani tsiku lotsatira limene lasankhidwa kudzayambitsa maphunziro a Baibulo. Fotokozani zokumana nazo zolimbikitsa, funsani wofalitsa kuti afotokoze maulaliki amene wagwiritsa ntchito mogwira mtima m’gawo lanu. M’pempheni kuti achite chitsanzo pogwiritsa ntchito ena mwa mawu oyamba opezeka patsamba 13 pakamutu kakuti “Phunziro la Baibulo Lapanyumba,” m’buku la Kukambitsirana.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Ubwino Wolankhula Motsimikiza mu Utumiki. Kukambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 194 mpaka 196.

Nyimbo Na. 32

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena