Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/10 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 5
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 5
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 6/10 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa July 5

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 5

Nyimbo Na. 43

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 9 ndime 1-12 ndi bokosi patsamba 101a

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 7-8

Na. 1: 1 Mafumu 8:14-26

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Timachenjezedwa Kuti Sitiyenera Kudziona Ngati Anzeru? (Yes. 5:21)

Na. 3: Kodi Anthu Amapezadi Ufulu Akanyalanyaza Mfundo za M’Baibulo Zokhudza Kugonana? (rs tsa. 171 ndime 1-3)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 7

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Njira Zowonjezera Utumiki Wanu—Gawo 1. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, tsamba 111, ndime 1 mpaka tsamba 112, ndime 2. Funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri amene asamukira kudera lina kapena kuphunzira chinenero china n’cholinga chowonjezera utumiki wawo. Kodi amakumana ndi mavuto otani? Kodi banja lawo kapena mpingo unawathandiza bwanji? Kodi apeza madalitso otani?

Mph. 10: Thandizani Ophunzira Anu Kudzifufuza. Nkhani yokambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 261 ndime 1 mpaka kumapeto kwa tsamba 262.

Nyimbo Na. 47

[Mawu a M’munsi]

a Mungasankhe kukambirana bokosi kapena ayi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena