Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/10 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 16
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 16
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 8/10 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa August 16

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 16

Nyimbo Na. 44

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 11 ndime 1-9

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 1-4

Na. 1: 2 Mafumu 1:1-10

Na. 2: Kodi N’chifukwa Chiyani Chuma Sichingatibweretsere Chimwemwe Chosatha? (Mlaliki 5:10)

Na 3: Kodi Dzina la Mulungu Limapezeka Pati M’Mabaibulo Amene Anthu Amakonda Kugwiritsa Ntchito Masiku Ano? (rs tsa. 415 ndime 8 mpaka tsa. 417 ndime 8)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 9

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Thandizani Wophunzira Wanu Kukhala Wofalitsa. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, tsamba 78 ndime 3 mpaka kumapeto kwa tsamba 80.

Mph. 10: Thandizani Ena Kuona Phindu la Uthenga Wabwino. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 159. Pemphani omvera kuti afotokoze zinthu zimene anthu ambiri amada nazo nkhawa m’gawo lanu. Apempheni kuti afotokoze mmene tingawathandizire anthuwa tikamalalikira.

Mph. 10: “Chakudya cha pa Nthawi Yoyenera.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Lengezani tsiku la msonkhano wapadera ngati mukulidziwa.

Nyimbo Na. 20

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena