Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/10 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 9/10 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa September 20

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 20

Nyimbo Na. 37

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv Mutu 12 ndime 9-14

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 19-22

Na. 1: 2 Mafumu 20:1-11

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kukhala Ofatsa? (Mat. 5:5)

Na. 3: Kodi Zingatheke Bwanji Kuti Munthu Aziopa Yehova Ndiponso Kumukonda? (rs-CN tsa. 422 ndime 4 ndi 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 15

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Tinachita Bwanji Chaka Chathachi? Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira utumiki. Fotokozani zimene mpingo wanu unachita mu utumiki chaka chautumiki chathachi, makamaka zinthu zabwino zimene unakwanitsa kuchita, ndipo uyamikireni mpingowo. Konzani zakuti wofalitsa mmodzi kapena awiri adzafotokoze zinthu zolimbikitsa zimene anakumana nazo. Tchulani mfundo imodzi kapena ziwiri zimene mpingo wanu uyenera kugwirirapo ntchito chaka talowachi, ndipo fotokozani zimene zingathandize mpingo wanu kuwongolere m’chaka chimenechi.

Mph. 10: “Malangizo Okhudza Abale Amene Amakamba Nkhani pa Msonkhano wa Utumiki.” Nkhani yokambidwa ndi mkulu.

Mph. 10: Thandizani Mwana Wanu Kukhala Wofalitsa. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Gulu, tsamba 81 ndi 82, ndime 1. Funsani kholo lachitsanzo chabwino limene lili ndi mwana wamng’ono yemwe ndi wofalitsa wosabatizidwa. Kodi linathandiza bwanji mwanayo kuti apite patsogolo ndi kuyenerere kukhala wofalitsa?

Nyimbo Na. 41

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena