Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/10 tsamba 5
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 22

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 22
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 22
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 11/10 tsamba 5

Ndandanda ya Mlungu wa November 22

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 22

Nyimbo Na. 6

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 15 ndime 10-17, ndi bokosi la patsamba 177

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 1-5

Na. 1: 2 Mbiri 3:1-13

Na. 2: Kodi Yehova Anakhululukira Anthu Machimo Chikhristu Chisanayambe pa Maziko Otani? (Aroma 3:24, 25)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Mboni za Yehova Zimalalikira Kunyumba ndi Nyumba? (rs tsa. 277 ndime 2-5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 45

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Mabuku Ogawira M’mwezi wa December. Nkhani yokambirana ndi omvera. Fotokozani zimene zili m’mabukuwo, ndipo chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zosonyeza zimene tinganene pogawira mabukuwo.

Mph. 20: “Yesetsani Kucheza ndi Anthu Osakhulupirira Amene Akazi Kapena Amuna Awo Ndi Mboni.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Funsani wofalitsa amene ali pa banja yemwe poyamba anali wosakhulupirira. Kodi mpingo unamuthandiza bwanji kuti ayambe kuchita chidwi ndi choonadi?

Nyimbo Na. 16

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena