Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/10 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 29
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 29
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 11/10 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa November 29

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 29

Nyimbo Na. 21

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 15 ndime 18-23, ndi bokosi la patsamba 180a

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 6-9

Na. 1: 2 Mbiri 6:12-21

Na. 2: Kodi N’chifukwa Chiyani Mboni za Yehova Zimazunzidwa? (rs tsa. 278 ndime 2 ndi 3)

Na. 3: Zimene Tiyenera Kuchita Kuti “Tipitirize Kugonjetsa Choipa mwa Kuchita Chabwino” (Aroma 12:21)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 54

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: “Kupemphera Ndiponso Kusinkhasinkha N’kofunika Kwa Atumiki Achangu.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Pemphani omvera kuti afotokoze nthawi imene amasinkhasinkha.

Mph. 10: ‘Aliyense Apereke Chopereka kwa Yehova.’ Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera mu Nsanja ya Olonda ya November 15, 2010, masamba 20-21.

Mph. 10: Konzekerani Kugawira Magazini M’mwezi wa December. Nkhani yokambirana ndi omvera. Fotokozani zimene zili m’magaziniwo kwa mphindi imodzi kapena ziwiri. Kenako sankhani mitu iwiri kapena itatu, ndipo funsani omvera kuti afotokoze mafunso ndiponso malemba amene akhoza kugwiritsa ntchito pogawira magaziniwo. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungagawire magazini iliyonse.

Nyimbo Na. 46

[Mawu a M’munsi]

a Mungasankhe kukambirana bokosi kapena ayi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena