Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/10 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 27
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 27
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 12/10 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa December 27

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 27

Nyimbo Na. 31

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 17 ndime 1-10

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 25-28

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 33

Mph. 5: Zilengezo. “Kalendala ya 2011 ikutsindika kufunika kwa Kulambira kwa pabanja.” Nkhani.

Mph. 10: Kodi Kukhala ndi Autilaini mu Utumiki N’kothandiza Bwanji? Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki masamba 167 mpaka 168, ndime 1. Pogwiritsa ntchito magazini ya mwezi wotsatira, sonyezani wofalitsa akulankhula yekha kwa mphindi zingapo pokonzekera zimene akanene mu utumiki.

Mph. 10: Imvi Ndizo Chisoti Chachifumu cha Ulemerero. (Miy. 16:31) Nkhani yokambirana yochokera mu Nsanja ya Olonda ya January 15, 2005, tsamba 8-9. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene ayenera kuonera anthu okalamba a mu mpingo.

Mph. 10: Konzekerani Kugawira Magazini M’mwezi wa January. Nkhani yokambirana. Fotokozani zimene zili m’magaziniwo kwa mphindi imodzi kapena ziwiri. Kenako sankhani mitu iwiri kapena itatu, ndipo funsani omvera kuti afotokoze mafunso ndiponso malemba amene akhoza kugwiritsa ntchito pogawira magaziniwo. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungagawire magazini iliyonse.

Nyimbo Na. 4

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena