Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/10 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 3
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 3
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 12/10 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa January 3

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 3

Nyimbo Na. 6

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 17 ndime 11-22

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 29-32

Na. 1: 2 Mbiri 30:13-22

Na. 2: Kodi Yesu Khristu Anali Munthu Wabwino Chabe? (rs tsa. 424 ndime 2)

Na. 3: Mmene Anthu Amakhalira mu Ukapolo Chifukwa Choopa Imfa (Aheb. 2:15)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 14

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Tinapatulidwa Kuti Tichite Chifuniro Cha Yehova. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, tsamba 168, ndime 2 mpaka kumapeto kwa mutuwo.

Mph. 10: Muzilankhula Mwachibadwa Polalikira. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 128, ndime 1 mpaka tsamba 129 ndime 1. Mwachidule funsani wofalitsa waluso amene poyamba anali wamanyazi. N’chiyani chimamuthandiza kuti asamachite mantha kwambiri mu utumiki?

Nyimbo Na. 17

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena