Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/11 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 23
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 23
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 5/11 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa May 23

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 23

Nyimbo Na. 32 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 7 ndime 9-16 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Masalimo 19-25 (Mph. 10)

Na. 1: Salimo 23:1–24:10 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Ayuda Onse Adzatembenuzidwa Kuti Akhulupirire Khristu?—rs tsa. 44 ndime 1 ndi 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Lemba la Aroma 8:21 Lidzakwaniritsidwa Liti Ndiponso Motani? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 35

Mph. 10: Zilengezo. “Mmene Mungagwiritsire Ntchito Fomu Yakuti Kaonaneni Ndi Wachidwi Uyu (S-43).” Nkhani yokambirana.

Mph. 10: Mfundo Zitatu Zothandiza Kuti Mawu Oyamba Azikhala Ogwira Mtima. Nkhani yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 9 ndime 1. Mukamaliza kufotokoza mfundo za m’bukulo, chitani zitsanzo ziwiri zosonyeza mmene munganenere mawu oyamba pogawira buku logawira m’mwezi wa June.

Mph. 15: Kodi Mwayesapo? Nkhani yokambirana. Kambani nkhani yachidule yofotokoza mfundo za m’nkhani zaposachedwapa za mu Utumiki Wathu wa Ufumu. Nkhani zake ndi izi: “Kagwiritseni Bwino Ntchito,” “Nkhani Zatsopano Zoyambitsira Maphunziro a Baibulo,” (km 12/10) ndi “Mphatso Yothandiza Kwa Mabanja” (km 1/11). Pemphani omvera kuti afotokoze zimene achita poyesa kugwiritsira ntchito malangizo a m’nkhanizi ndiponso phindu limene apeza.

Nyimbo Na. 6 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena