Ndandanda ya Mlungu wa May 23
MLUNGU WOYAMBIRA MAY 23
Nyimbo Na. 32 ndi Pemphero
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cf mutu 7 ndime 9-16 (Mph. 25)
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: Masalimo 19-25 (Mph. 10)
Na. 1: Salimo 23:1–24:10 (Osapitirira mph. 4)
Na. 2: Kodi Ayuda Onse Adzatembenuzidwa Kuti Akhulupirire Khristu?—rs tsa. 44 ndime 1 ndi 2 (Mph. 5)
Na. 3: Kodi Lemba la Aroma 8:21 Lidzakwaniritsidwa Liti Ndiponso Motani? (Mph. 5)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 10: Zilengezo. “Mmene Mungagwiritsire Ntchito Fomu Yakuti Kaonaneni Ndi Wachidwi Uyu (S-43).” Nkhani yokambirana.
Mph. 10: Mfundo Zitatu Zothandiza Kuti Mawu Oyamba Azikhala Ogwira Mtima. Nkhani yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 9 ndime 1. Mukamaliza kufotokoza mfundo za m’bukulo, chitani zitsanzo ziwiri zosonyeza mmene munganenere mawu oyamba pogawira buku logawira m’mwezi wa June.
Mph. 15: Kodi Mwayesapo? Nkhani yokambirana. Kambani nkhani yachidule yofotokoza mfundo za m’nkhani zaposachedwapa za mu Utumiki Wathu wa Ufumu. Nkhani zake ndi izi: “Kagwiritseni Bwino Ntchito,” “Nkhani Zatsopano Zoyambitsira Maphunziro a Baibulo,” (km 12/10) ndi “Mphatso Yothandiza Kwa Mabanja” (km 1/11). Pemphani omvera kuti afotokoze zimene achita poyesa kugwiritsira ntchito malangizo a m’nkhanizi ndiponso phindu limene apeza.
Nyimbo Na. 6 ndi Pemphero