Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/12 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 6
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 6
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 1/12 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa February 6

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 6

Nyimbo Na. 45 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 1 ndime 16-21 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 47-51 (Mph. 10)

Na. 1: Yesaya 51:1-11 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Mwambo wa Ukwati wa Adamu ndi Hava Unali Wotani?—rs tsa. 384 ndime 1-2 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Mulungu, Yemwe Ndi Wachikondi, Adzawononge Anthu Ena?—2 Ates. 1:6-9 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 36

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Malo Ochezera a pa Intaneti?—Gawo 2. Nkhani yochokera mu Galamukani! ya August 2011, masamba 10 mpaka 13 ndi Galamukani! ya February 2012, tsamba 8 ndi 9.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Zimene Munganene Pogawira Magazini M’mwezi wa Februaryy. Nkhani yokambirana. Kwa mphindi imodzi kapena ziwiri, fotokozani nkhani zochepa za m’magaziniwo zimene zingakhale zogwira mtima kwa anthu a m’gawo lanu. Kenako, pogwiritsa ntchito nkhani zoyambirira mu Nsanja ya Olonda, pemphani omvera kuti afotokoze mafunso okopa chidwi amene angagwiritse ntchito ndiponso malemba amene angawerenge. Chitaninso chimodzimodzi ndi nkhani zoyambirira za mu Galamukani! Ndipo ngati nthawi ilipo fotokozaninso nkhani imodzi. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungagawirire magazini iliyonse.

Nyimbo Na. 96 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena