Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/12 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 30
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 30
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 4/12 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa April 30

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 30

Nyimbo Na. 63 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 5 ndime 9-16 ndi bokosi patsamba 41 ndi 42 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yeremiya 32-34 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 82

Mph. 10: Zilengezo. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 4, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka loyambirira m’mwezi wa May.

Mph. 10: Mmene Mungayankhire Anthu Amene Amakana Kukambirana za Chipembedzo. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 91 ndime 3 mpaka tsamba 94 ndime 2. Chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zachidule.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Machitidwe 4:1-13, 18-20. Kambiranani mmene mavesi amenewa angatithandizire mu utumiki.

Mph. 5: “Timakobidi Tiwiri Tochepa Mphamvu.” Nkhani.

Nyimbo Na. 126 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena