Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/12 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 24
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 24
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 9/12 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa September 24

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 24

Nyimbo Na. 49 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 12 ndime 14-20 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Danieli 1-3 (Mph. 10)

Na. 1: Danieli 2:17-30 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Angelo Amachita Zinthu Mwadongosolo?—rs tsa. 139 ndime 2 mpaka tsa. 140 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingapewe Bwanji Kumvetsa Chisoni Mzimu wa Yehova?—Aef. 4:30 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 130

Mph. 30: “Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa—Kodi Ndidzachite Zotani Pamoyo Wanga? (Gawo 2)” Mafunso ndi mayankho. M’mawu oyamba, osapitirira mphindi imodzi, nenani mwachidule zimene tinakambirana mlungu watha pa Gawo 1 la nkhaniyi. Pomaliza nkhaniyi, yamikirani achinyamata chifukwa choyesetsa ‘kukumbukira’ Yehova pa unyamata wawo. (Mlal. 12:1) Alimbikitseni kuti apitirize kugwiritsira ntchito moyo wawo potumikira Yehova.

Nyimbo Na. 91 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena