Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 15

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 15
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 15
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa October 15

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 15

Nyimbo Na. 29 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 13 ndime 17-24 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Danieli 10-12 (Mph. 10)

Na. 1: Danieli 11:15-27 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Akhristu Sabwezera Ena Akawachitira Zoipa?—Aroma 12:18-21 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Atumiki Okhulupirika a Mulungu Akupezeka M’Matchalitchi Osiyanasiyana Achikhristu?—rs tsa. 142 ndime 3-5 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 106

Mph. 10: Ngati Wina Wanena Kuti ‘Sindikufuna Kukambirana za M’Baibulo.’ Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 16, ndime 1 mpaka tsamba 18 ndime 1. Kambiranani zina mwa mfundo zimene zili m’bukuli komanso mfundo zina zimene zakhala zothandiza m’gawo la mpingo wanu. Chitani zitsanzo ziwiri zachidule.

Mph. 20: “Muzigwiritsa Ntchito Timapepala Pofalitsa Uthenga Wabwino.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana ndime yachisanu, fotokozani mwachidule zimene zili m’timapepala timene tidzagawire mwezi wa November ndipo muchite chitsanzo. Mukamakambirana ndime 7, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito timapepala polalikira mwamwayi.

Nyimbo Na. 97 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena