Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsamba 5
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 29
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 29
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsamba 5

Ndandanda ya Mlungu wa October 29

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 29

Nyimbo Na. 125 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 14 ndime 6-10 ndi bokosi patsamba 110 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Hoseya 8-14 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 108

Mph. 15: “Zimene Mungachite Kuti Muzipindula ndi Kagulu Kanu ka Utumiki.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana bokosi la patsamba 6, funsani mwachidule munthu amene msonkhano wokonzekera utumiki wakumunda umachitikira panyumba yake. Kodi amachita chiyani kuti pokonzekera msonkhano umenewu mlungu uliwonse? N’chifukwa chiyani amayamikira mwayi umene ali nawo, woti msonkhanowu umachitikira pakhomo lake?

Mph. 15: “Njira Zisanu Zopezera Phunziro la Baibulo.” Mafunso ndi mayankho. Mukamaliza kukambirana ndime 6, funsani abale ndi alongo amene anachititsapo phunziro la Baibulo lopita patsogolo kuti afotokoze mwachidule madalitso amene anapeza.

Nyimbo Na. 122 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena