Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsamba 7
  • Nkhani Zatsopano Zimene Zizipezeka mu Nsanja ya Olonda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zatsopano Zimene Zizipezeka mu Nsanja ya Olonda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Alimbikitseni Kuti Aziyambitsa Maphunziro a Baibulo Loweruka Loyambirira la Mwezi
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Zatsopano Zoyambitsira Maphunziro A Baibulo
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Nkhani Zothandiza mu Utumiki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Magazini Yophunzira Yatsopano ya Nsanja ya Olonda
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsamba 7

Nkhani Zatsopano Zimene Zizipezeka mu Nsanja ya Olonda

Loweruka loyambirira la mwezi uliwonse, takhala tikugwiritsa ntchito nkhani za mu Nsanja ya Olonda zakuti, “Phunzirani Zimene Mawu a Mulungu Amanena” poyambitsa maphunziro a Baibulo. Kuyambira mu January, nkhanizi zilowedwa m’malo ndi nkhani zakuti, “Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,” ndipo zizikhala kuchikuto chomaliza cha magazini yogawira. Tizigwiritsa ntchito nkhani zakuti “Kuyankha Mafunso a M’Baibulo” mu utumiki mofanana ndi mmene tinkachitira ndi nkhani zakuti, “Phunzirani Zimene Mawu a Mulungu Amanena.” (km 12/10 tsamba 2) Monga mmene zinalili m’mbuyomu, Utumiki Wathu wa Ufumu uzikhala ndi chitsanzo cha ulaliki chimene tizidzagwiritsa ntchito Loweruka loyambirira la mwezi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena