Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/13 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 23
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 23
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 12/13 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa December 23

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 23

Nyimbo Na. 106 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 5 ndime 7-12 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Chivumbulutso 7-14 (Mph. 10)

Na. 1: Chivumbulutso 9:1-21 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Akhristu Angasonyeze Bwanji Kuti Ndi Ochereza?—Aheb. 13:2 (Mph. 5)

Na. 3: Akhristu a mu Chipembedzo Choona Amakondana Komanso Sakhala Mbali ya Dziko—rs tsa. 90 ndime 2-3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 124

Mph. 10: Mabuku Ogawira mu January ndi February. Nkhani yokambirana. Fotokozani zimene zili m’mabukuwo ndipo chitani zitsanzo ziwiri zosonyeza mmene tingawagawirire.

Mph. 20: “Kodi Tingawathandize Bwanji?” Mafunso ndi mayankho. Chitani chitsanzo chimodzi pogwiritsa ntchito mfundo zimene zili patsamba 6.

Nyimbo Na. 46 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena