Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/15 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 19
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 19
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 1/15 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa January 19

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 19

Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 7 ndime 9-17 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 1-4 (Mph. 8)

Na. 1: Oweruza 3:1-11 (Osapitirira mph. 3)

Na. 2: Yehova Amadana ndi Chinyengo—bt tsa. 35 ndime 18-20 (Mph. 5)

Na. 3: Yehova Akhoza Kulepheretsa Mapulani a Anthu Oipa Ngati Ahitofeli—2 Sam. 16:23; 17:1-14 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

MUTU WA MWEZI UNO: ‘Tumikirani Ambuye Monga Kapolo Modzichepetsa Kwambiri.’—Mac. 20:19.

Nyimbo Na. 77

Mph. 10: Kodi Mukugwiritsa Ntchito Zakumapeto mu Baibulo la Dziko Latsopano? Nkhani yokambirana. Kodi tingagwiritse ntchito bwanji Zakumapeto zomwe zili mu Baibulo la Dziko Latsopano kuti tithandize munthu amene tikuphunzira naye Baibulo kumvetsa zokhudza (a) Gehena (b) Manda a anthu onse (Sheoli, Hade) (c) Dama.

Mph. 10: Kutumikira Mulungu Monga Kapolo Kumafuna Khama Komanso Kudzipereka. Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2014, tsamba 59 ndime 1 mpaka tsamba 62 ndime 1 komanso tsamba 67 ndime 2. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Mph. 10: “Pitirizani Kuwonjezera Luso Lanu Lophunzitsa.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 20 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena