Ndandanda ya Mlungu wa January 19
MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 19
Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero
Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cl mutu 7 ndime 9-17 (Mph. 30)
Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: Oweruza 1-4 (Mph. 8)
Na. 1: Oweruza 3:1-11 (Osapitirira mph. 3)
Na. 2: Yehova Amadana ndi Chinyengo—bt tsa. 35 ndime 18-20 (Mph. 5)
Na. 3: Yehova Akhoza Kulepheretsa Mapulani a Anthu Oipa Ngati Ahitofeli—2 Sam. 16:23; 17:1-14 (Mph. 5)
Msonkhano wa Utumiki:
MUTU WA MWEZI UNO: ‘Tumikirani Ambuye Monga Kapolo Modzichepetsa Kwambiri.’—Mac. 20:19.
Mph. 10: Kodi Mukugwiritsa Ntchito Zakumapeto mu Baibulo la Dziko Latsopano? Nkhani yokambirana. Kodi tingagwiritse ntchito bwanji Zakumapeto zomwe zili mu Baibulo la Dziko Latsopano kuti tithandize munthu amene tikuphunzira naye Baibulo kumvetsa zokhudza (a) Gehena (b) Manda a anthu onse (Sheoli, Hade) (c) Dama.
Mph. 10: Kutumikira Mulungu Monga Kapolo Kumafuna Khama Komanso Kudzipereka. Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2014, tsamba 59 ndime 1 mpaka tsamba 62 ndime 1 komanso tsamba 67 ndime 2. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.
Mph. 10: “Pitirizani Kuwonjezera Luso Lanu Lophunzitsa.” Mafunso ndi mayankho.
Nyimbo Na. 20 ndi Pemphero