Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/15 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 22

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 22
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 22
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 6/15 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa June 22

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 22

Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 14 ndime 16-20 ndi bokosi patsamba 147 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 1-2 (8 min.)

Na.  1: 1 Mafumu 1:15-27 (Osapitirira 3 min.)

Na.  2: N’chifukwa Chiyani Akhristu Oona Amakhala Osangalala?—igw tsa. 23 ndime 1-3 (5 min.)

Na.  3: Zimene Mungachite Kuti Yehova Akudalitseni mu Utumiki—bt tsa. 126-127 ndime 5-8 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: “Kumbukirani masiku akale”—Deut. 32:7.

Nyimbo Na. 75

15 min: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana yokambidwa ndi mlembi. Fotokozani zimene abale ndi alongo anachita pa nyengo ya Chikumbutso ndipo ayamikireni chifukwa cha zimene anachita. Pemphani omvera kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zimene anakumana nazo pamene ankagawira timapepala toitanira anthu ku Chikumbutso.

15 min: Kodi Yehova Anakugwirani Bwanji Dzanja? (Yes. 41:13) Funsani munthu mmodzi kapena awiri amene akhala akutumikira mokhulupirika kwa nthawi yaitali. Kodi Yehova amawathandiza bwanji kupirira mavuto amene akukumana nawo pamene akumutumikira.

Nyimbo Na. 107 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena