Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/15 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 5
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 5
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 9/15 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 5

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 5

Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 19 ndime 18-23 ndi bokosi patsamba 198 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 1-4 (8 min.)

Na. 1: 1 Mbiri 1:28-42 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Tizikhala Okonzeka Kuuza Ena za Yehova—bt tsa. 140-141 ndime 4-5 (5 min.)

Na. 3: Kodi Wokana Khristu Ndi Ndani?—rs tsa. 414, Tanthauzo ndiponso ndime 1-2 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: ‘Muzichitira umboni mokwanira za uthenga wabwino.’—Mac. 20:24.

Nyimbo Na. 82

10 min: Zimene Munganene Pogawira Magazini a October. Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuchita zitsanzo ziwiri zosonyeza zimene tinganene pogawira magaziniwa pogwiritsa ntchito zitsanzo zaulaliki zomwe zili patsamba lino. Kenako kambiranani chitsanzo cha ulaliki chilichonse kuyambira poyambirira mpaka pamapeto.

10 min: Zofunika pampingo.

10 min: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene anapindulira pogwiritsa ntchito malangizo a m’nkhani yakuti, “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Kulalikira M’gawo Lamalonda.” Kenako apempheni kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zomwe anakumana nazo.

Nyimbo Na. 98 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena