Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/15 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 28
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 28
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 12/15 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa December 28

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 28

Nyimbo Na. 1 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 23 ndime 19-23 ndi bokosi patsamba 239 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 25-28 (8 min.)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (20 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezu Uno: “Tiyenera kukumana ndi masautso ambiri kuti tikalowe mu Ufumu wa Mulungu.”—Mac. 14:22.

Nyimbo Na. 122

15 min: Tizipempherera Abale Athu. Nkhani yokambirana. Poyamba werengani Machitidwe 12:1-11. Ndiyeno kambiranani mfundo zothandiza zimene zili m’buku lakuti Kuchitira Umboni, tsamba 77-80, ndime 5-12. Kenako kambiranani nkhani zatsopano zimene zili pa webusaiti yathu pamene alemba kuti “Malo a Nkhani” kapena onani m’mabuku athu atsopano. Limbikitsani onse kuti azipempherera abale ndi alongo athu amene akukumana ndi mavuto osiyanasiyana ndipo ngati n’kotheka akhoza kumatchula mayina awo m’pemphero.—2 Akor. 1:11; 1 Tim. 2:1, 2.

15 min: Zofunika pampingo.

Nyimbo Na. 124 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena