Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 February tsamba 2
  • Kumvera Yehova Kumabweretsa Madalitso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kumvera Yehova Kumabweretsa Madalitso
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Mmene Mungakumanire ndi Mtendere wa Umulungu Mokwanira Kwambiri?
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Mukhoza Kupeza Nzeru
    Galamukani!—2021
  • Yehova Amakwaniritsa Zomwe Walonjeza
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Anthu a Yehova Amakonda Chilungamo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 February tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YESAYA 47-51

Kumvera Yehova Kumabweretsa Madalitso

48:17

  • Yehova amatisonyeza mwachikondi ‘njira imene tiyenera kuyendamo’ n’cholinga choti tizikhala osangalala. Tikamamumvera zinthu zimatiyendera bwino.

“Mtendere . . . ngati mtsinje”

48:18

  • Yehova akulonjeza kuti tingakhale ndi mtendere wochuluka ndiponso wosatha ngati mtsinje womwe susiya kuyenda

“Chilungamo . . . ngati mafunde a m’nyanja”

  • Tidzatha kuchita zinthu zachilungamo zosawerengeka ngati mafunde a m’nyanja

Madzi akuyenda mumtsinje komanso panyanja pali mafunde
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena