Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 February tsamba 3
  • February 13-19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • February 13-19
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 February tsamba 3

February 13-19

YESAYA 52-57

  • Nyimbo Na. 148 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Khristu Anavutika Chifukwa cha Ife”: (10 min.)

    • Yes. 53:3-5​—Ananyozedwa ndiponso kuphwanyidwa chifukwa cha zochimwa zathu (w09 1/15 26 ¶3-5)

    • Yes. 53:7, 8​—Anapereka yekha moyo wake kuti atipulumutse (w09 1/15 27 ¶10)

    • Yes. 53:11, 12​—Popeza kuti Yesu anakhala wokhulupirika mpaka imfa, tili ndi mwayi woti Mulungu akhoza kutiona kuti ndife olungama (w09 1/15 28 ¶13)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yes. 54:1​—Kodi “mkazi wosabereka” amene akutchulidwa mu ulosiwu ndi ndani, nanga “ana” ake ndi ndani? (w06 3/15 11 ¶2)

    • Yes. 57:15​—Kodi Yehova “amakhala” bwanji ndi anthu “opsinjika” ndiponso “onyozeka”? (w05 10/15 26 ¶3)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yes. 57:1-11

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) bm​—Siyani funso loti mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) bm 30-31​—Siyani funso loti mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 13-14 ¶16-17​—Ngati n’zotheka, chitsanzochi chikhale cha bambo akuphunzira ndi mwana wake.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 110

  • “Muzithandiza Ana Anu Kuti Azikhulupirira Kwambiri Mlengi”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Zimene Achinyamata Anzanu Amanena​—Kukhulupirira Kuti Kuli Mulungu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 17 ¶14-22 komanso Mfundo Zofunika Kuziganizira patsamba 152

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 107 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena