Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsamba 2
  • “Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndaika Mawu Anga M’kamwa Mwako”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • “Sindingathe Kukhala Chete”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Yeremiya—Mneneri Wachilendo wa Ziweruzo za Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • “Tsopano Uwauze” Mawu Awa
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 March tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 1-4

“Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”

Losindikizidwa

N’kutheka kuti Yeremiya anali ndi zaka pafupifupi 25 pamene Yehova anamuika kukhala mneneri. Yeremiya ankaona kuti sangakwanitse ntchito imeneyi, koma Yehova anamutsimikizira kuti amuthandiza.

Mneneri Yeremiya wamangidwa m’matangadza, akumutulutsa m’chitsime komanso akulira chifukwa cha kuwonongedwa kwa Yerusalemu
  1. 647

    Yeremiya anaikidwa kukhala mneneri

  2. 607

    Yerusalemu anawonongedwa

  3. 580

    Nthawi imene anamaliza kulemba bukuli

Zaka zonsezi ndi za B.C.E.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena