Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 June tsamba 6
  • June 25–July 1

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 25–July 1
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 June tsamba 6

June 25–July 1

Luka 4-5

  • Nyimbo Na. 37 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Muzitsanzira Yesu Pokana Mayesero”: (10 min.)

    • Luka 4:1-4​—Yesu sanalole kuti chilakolako cha thupi chimugonjetse (w13 8/15 25 ¶8)

    • Luka 4:5-8​—Yesu sanakopeke ndi chilakolako cha maso (w13 8/15 25 ¶10)

    • Luka 4:9-12​—Yesu sanagonje pamene anayesedwa kuti achite zinthu modzionetsera [Onerani vidiyo yakuti Pamwamba pa Khoma la Mpanda wa Kachisi.] (“Pamwamba pa Khoma la Mpanda wa Kachisi” zithunzi ndi mavidiyo pa Luka 4:9, nwtsty; w13 8/15 26 ¶12)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Luka 4:17​—Kodi n’chiyani chikusonyeza kuti Yesu ankadziwa bwino Mawu a Mulungu? (“mpukutu wa mneneri Yesaya” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 4:17, nwtsty)

    • Luka 4:25​—Kodi chilala chimene chinachitika m’nthawi ya Eliya chinatenga nthawi yaitali bwanji? (“zaka zitatu ndi miyezi 6” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 4:25, nwtsty)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Luka 4:31-44

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha zimene tinganene. Kenako musiyireni khadi lodziwitsa anthu za JW.ORG.

  • Ulendo Wobwereza Wachitatu: (Osapitirira 3 min.) Sankhani lemba lililonse ndipo gawirani buku kapena kabuku kamene timagwiritsa ntchito pophunzira ndi anthu.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) jl mutu 28

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 28

  • “Muzisamala Mukamacheza ndi Anzanu pa Intaneti”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muzichita Zinthu Mwanzeru Mukamacheza ndi Anzanu pa Intaneti.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 20 ¶17-19 komanso tsamba 216, 217, 218-219

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 105 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena