Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsamba 2
  • January 7-13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • January 7-13
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 January tsamba 2

January 7-13

MACHITIDWE 21-22

  • Nyimbo Na. 55 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Chifuniro cha Yehova Chichitike”: (10 min.)

    • Mac. 21:8-12​—Akhristu anzake a Paulo anamupempha kuti asapite ku Yerusalemu chifukwa cha mavuto amene ankayembekezera kukakumana nawo kumeneko (bt 177-178 ¶15-16)

    • Mac. 21:13​—Paulo anali wofunitsitsa kuchita zimene Yehova ankafuna (bt 178 ¶17)

    • Mac. 21:14​—Abale ataona kuti Paulo watsimikiza mtima, anasiya kumuletsa (bt 178 ¶18)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mac. 21:23, 24​—N’chifukwa chiyani akulu a ku Yerusalemu anauza Paulo malangizo amenewa ngakhale kuti pa nthawiyi Akhristu sanalinso pansi pa Chilamulo cha Mose? (bt 184-185 ¶10-12)

    • Mac. 22:16​—Kodi kubatizidwa kwa Paulo kunachotsa bwanji machimo ake? (“kusamba kuti uchotse machimo ako mwa kuitana pa dzina lake” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mac. 22:16, nwtsty)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mac. 21:1-19 (th phunziro 5)a

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Mawu Oyamba Abwino, kenako kambiranani mfundo za m’phunziro 1 m’kabuku ka Kuphunzitsa.

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) w10 2/1 13 ¶1 mpaka 14 ¶2​—Mutu: Kodi Akhristu Ayenera Kusunga Sabata? (th phunziro 1)b

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 134

  • “Yehova Anatithandiza Kulera Ana Athu”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 20

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 66 ndi Pemphero

a b Dziwani izi: Kuyambira mwezi uno, Ndandanda ya Utumiki izikhala ndi phunziro limene wophunzira wapatsidwa lomwe lizikhala kutsogolo kwa nkhani yake mumkutira mawu. Phunziroli lizichokera m’kabuku kakuti Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso (th).

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena