Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 November tsamba 6
  • Anthu 4 Okwera Pamahatchi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anthu 4 Okwera Pamahatchi
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Mawu Oyamba
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Kodi Ulosi wa Anthu 4 Okwera Pamahatchi Umakukhudzani Bwanji Inuyo?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Kodi Anthu 4 Okwera Pamahatchi Akuimira Chiyani?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 November tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | CHIVUMBULUTSO 4-6

Anthu 4 Okwera Pamahatchi

6:2, 4-6, 8

Yesu wakwera hatchi yoyera ndipo akukoka uta; pambuyo pake pakubwera hatchi yofiira, yakuda komanso yotuwa

Yesu ‘anapita kukagonjetsa adani ake’ pamene anamenya nkhondo yolimbana ndi Satana komanso ziwanda zake n’kuwagwetsera padziko lapansi. Iye akupitirizabe kugonjetsa adani ake pothandiza komanso kuteteza atumiki ake m’masiku otsiriza ano. Komabe adzamaliza ntchito yolimbana ndi adaniwo akadzagonjetsa okwera pamahatchi atatu enawo. Iye adzachita zimenezi pankhondo ya Aramagedo ndipo kenako adzakonza zonse zomwe okwera pamahatchi atatu aja anawononga.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena