Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsamba 4
  • Mavuto Omwe Anabwera Chifukwa cha Bodza Loyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mavuto Omwe Anabwera Chifukwa cha Bodza Loyamba
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Anakunamizani?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • “Dzina Lanu Liyeretsedwe”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • Choonadi Ponena za Bodza
    Galamukani!—1997
  • Chiphunzitso Chaumulungu Chilimbana ndi Ziphunzitso za Ziŵanda
    Nsanja ya Olonda—1994
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 January tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 3-5

Mavuto Omwe Anabwera Chifukwa cha Bodza Loyamba

3:1-6, 15-19

Chithunzi choyamba: Satana akulankhula ndi Hava pogwiritsa ntchito njoka. Chachiwiri: Adamu ndi Hava akalamba ndipo akuoneka ofooka. Chachitatu: Mzera wa anthu kuchokera pa Adamu ndi Hava kudzafika m’nthawi yathu, zomwe zikuimira nyengo zosiyanasiyana, mitundu komanso zikhalidwe.

Satana wakhala akusocheretsa anthu kungochokera pamene ananamiza Hava. (Chiv. 12:9) Kodi mabodza a Satana otsatirawa amalepheretsa bwanji anthu kukhala pa ubwenzi ndi Yehova?

  • Kunja kuno kulibe Mulungu

  • Pali milungu itatu mwa Mulungu mmodzi

  • Mulungu alibe dzina

  • Mulungu amawotcha anthu ku Gehena kwamuyaya

  • Chilichonse chimene chimachitika ndi chifuniro cha Mulungu

  • Mulungu alibe nafe ntchito

Kodi mumamva bwanji mukamva mabodza amenewa?

Nanga mungathandize bwanji kuyeretsa dzina la Mulungu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena