Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsamba 4
  • January 13-19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • January 13-19
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 January tsamba 4

JANUARY 13-19

GENESIS 3-5

  • Nyimbo Na. 72 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mavuto Omwe Anabwera Chifukwa cha Bodza Loyamba”: (10 min.)

    • Gen. 3:1-5​—Mdyerekezi ananenera Mulungu zabodza (w17.02 5 ¶9)

    • Gen. 3:6​—Adamu ndi Hava sanamvere Mulungu (w00 11/15 25-26)

    • Gen. 3:15-19​—Mulungu anawapatsa chilango (w12 9/1 4 ¶2; w04 1/1 29 ¶2; it-2 186)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 4:23, 24​—N’chifukwa chiyani Lameki anapeka ndakatuloyi? (it-2 192 ¶5)

    • Gen. 4:26​—Kodi anthu a m’nthawi ya Inosi anayamba “kuitanira pa dzina la Yehova” m’njira yotani? (it-1 338 ¶2)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 4:17–5:8 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: N’chiyani chakusangalatsani ndi mmene wofalitsayu anayambira kukambirana ndi mwininyumba? Kodi tikuphunzirapo chiyani pa zimene ofalitsawa achita pokonza zoti adzapange ulendo wobwereza?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 1)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 3)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako musiyireni magazini yatsopano yomwe ili ndi nkhani imene mwininyumba anatchula. (th phunziro 2)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 63

  • “Kodi Tingayambe Bwanji Kukambirana ndi Anthu Pogwiritsa Ntchito Timapepala?”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonera vidiyo yomwe ikusonyeza zimene tingachite kuti tiyambe kukambirana ndi anthu pogwiritsa ntchito timapepala. Kenako kambiranani zimene mukuphunzirapo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 68

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 70 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena