Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwbq nkhani 21
  • Kodi Mdyerekezi Ndi Amene Amachititsa Mavuto Onse?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mdyerekezi Ndi Amene Amachititsa Mavuto Onse?
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yankho la m’Baibulo
  • Kodi Amene Akulamulira Dzikoli Ndani Kwenikweni?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Mdani wa Moyo Wosatha
    Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
Onani Zambiri
Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
ijwbq nkhani 21
Dzanja la Mdyerekezi lagwira dziko lapansi

Kodi Mdyerekezi Ndi Amene Amachititsa Mavuto Onse?

Yankho la m’Baibulo

Baibulo limasonyeza kuti Satana Mdyerekezi ndi munthu weniweni. Iye ali ngati mtsogoleri wa zigawenga wamphamvu kwambiri amene amagwiritsa ntchito “zizindikiro zabodza” ndiponso “chinyengo” pofuna kukwaniritsa zolinga zake. Ndipotu Baibulo limati iye “amadzisandutsa mngelo wa kuwala.” (2 Atesalonika 2:9, 10; 2 Akorinto 11:14) Zinthu zoipa zimene iye amachita zimapereka umboni wakuti Satanayo alipodi.

Komabe, sikuti Mdyerekezi ndi amene amachititsa mavuto onse. N’chifukwa chiyani tikutero? Mulungu analenga anthu m’njira yakuti azitha kusankha pakati pa chabwino ndi choipa. (Yoswa 24:15) Choncho, tikasankha zinthu mopanda nzeru timakumana ndi mavuto.—Agalatiya 6:7, 8.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena