B12-B
Wiki Yomaliza ya Moyo wa Yesu Padziko Lapansi (Gawo 2)
Yerusalemu ndi Madera Ozungulira
Kachisi
Munda wa Getsemane (?)
Nyumba ya Bwanamkubwa
Nyumba ya Kayafa (?)
Nyumba imene Herode Antipa ankakhala (?)
Damu la Betizata
Dziwe la Siloamu
Holo ya Khoti Lalikulu la Ayuda (?)
Gologota (?)
Munda Wamagazi (?)
Sankhani tsiku: Nisan 12 | Nisan 13 | Nisan 14 | Nisan 15 | Nisan 16
Nisani 12
MADZULO (Masiku a Ayuda amayamba ndi kutha dzuwa litalowa)
M’MAWA
Yesu ndi ophunzira ake
Yudasi anakonza zoti apereke Yesu
MADZULO
Nisani 13
MADZULO
M’MAWA
Petulo ndi Yohane akukonzekera Pasika
Yesu ndi atumwi ake ena anafika madzulo
MADZULO
Nisani 14
MADZULO
Anadya Pasika ndi atumwi ake
Anasambitsa mapazi a atumwi ake
Anauza Yudasi kuti achoke
Anayambitsa mwambo wa Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
Nisani 15 (Sabata)
MADZULO
Nisani 16
M’MAWA
Anaukitsidwa
Anaonekera kwa ophunzira ake