Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 9/8 tsamba 31
  • Mabuku Aulere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mabuku Aulere
  • Galamukani!—1990
  • Nkhani Yofanana
  • Mphamvu Zimene Manyuzipepala Ali Nazo
    Galamukani!—2005
  • Kuuza Anthu Nkhani
    Galamukani!—2005
  • Gawirani Magazini mu Utumiki Wanu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
  • Magazini Amalengeza Ufumu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
Onani Zambiri
Galamukani!—1990
g90 9/8 tsamba 31

Mabuku Aulere

MANYUZIPEPALA aulere mu Briteni akubweretsa ndalama zosatsira malonda madola mamiliyoni mazana angapo m’kufalitsidwa kwa makope ake mamiliyoni makumi ambiri pamlungu. Zotulukapo zake zaposadi kutalitali kalambula bwalo wochepa amene anakundika zaka 20 zapitazo. “Anthu anaseka lingaliro la kusatsira malonda m’chinthu chaulere,” anatero Ian Locks, mtsogoleri wamkulu wa Association of Free Newspapers. Koma, kwenikweni, “iyo yayamba kugaŵira manyuzipepala ake onse mwaulere, magazine ndi timabuku monga mtundu watsopano wa mwaŵi wa zamalonda,” iye waonjezera tero.

Magazinenso? Inde. Magazine osiyanasiyana oposa 400 amagaŵiridwa mwaulere mu United Kingdom, amagaŵiridwanso mamiliyoni makumi ambiri. Mtengo wake wochepa wakoka osatsa malonda a manyuzipepala a kumaloko, kumene ambiri a awa akugaŵiridwa aulere. The Times ya ku London ikufotokoza kampaniyi kukhala “magwero amphamvu atsopano mu indasitale yofalitsa ya ku Briteni,” yomwe idzakhalitsa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena