Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g02 2/8 tsamba 1-3
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2002
  • Nkhani Yofanana
  • Tizithandiza Alendo Kuti ‘Azitumikira Yehova Mokondwera’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Ziŵerengero Zomawonjezereka za Othaŵa Kwawo
    Galamukani!—1996
  • Kodi Chothetsera Chake Nchiyani?
    Galamukani!—1996
  • Dziko Limene Aliyense Angaloledwe Kudzakhalamo
    Galamukani!—2002
Onani Zambiri
Galamukani!—2002
g02 2/8 tsamba 1-3

Zamkatimu

February 8, 2002

Kodi Othaŵa Nkhondo Adzapezadi Malo Okhazikika?

Padziko lonse, anthu othaŵa kwawo amangoyendayenda atasoŵa pogwira. Anthu ambiri pa gululi sapeza n’komwe bata limene amafunafunalo. Kodi ilipo nthaŵi ina imene aliyense adzakhaleko ndi malo omati ndiye kwawo?

3 Anthu Amene Akufunafuna Bata

6 Kupeza Malo Amene Angamati Ndiye Kwawo

11 Dziko Limene Aliyense Angaloledwe Kudzakhalamo

14 Mbidzi—Hatchi ya mu Africa Yongodziyendera Mmene Ikufunira

21 “Tsiku Losangalatsa Kwambiri M’moyo Wathu”

22 Tsiku Laukwati N’losangalatsa Komanso N’losautsa

27 Ukwati Uyenera Kukhala Mgwirizano Wosatha

32 “Chonde Ndithandizeni! Ndinu Nokha Amene Ndikudalira”

Kodi Pali Vuto Ngati Nditachitako Chidwi Pang’ono Ndi Zamatsenga? 18

Achinyamata ambiri amachita chidwi ndi zamatsenga. Kodi n’zosangalatsadi kapena zikhoza kum’vulaza munthu?

Kodi Mikaeli Mngelo Wamkulu Ndani? 30

M’Baibulo angelo aŵiri okha ndi amene anawatchula mayina awo. Tiyeni tim’dziŵe mngelo weniweni wotchedwa Mikaeli.

[Chithunzi pachikuto]

Pa chikuto: Othaŵa nkhondo a ku Rwanda akubwerera kwawo

[Mawu a Chithunzi]

UNHCR/R. Chalasani

[Chithunzi pamasamba 2, 3]

Pa masamba 2 ndi 3: Othaŵa kwawo a ku Ethiopia akudikirira kulandira chakudya ndi madzi

[Mawu a Chithunzi]

UN PHOTO 164673/JOHN ISAAC

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena