Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 5/07 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2007
  • Nkhani Yofanana
  • Kuchokera kwa Owerenga
    Galamukani!—2008
  • Posachedwapa, Sikudzakhalanso Mmphaŵi!
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Tsanzirani Yesu Poganizira Osauka
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Limbikitsani Osauka
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
Onani Zambiri
Galamukani!—2007
g 5/07 tsamba 1-2

Zamkatimu

May 2007

Kulimbana ndi Umphawi M’dziko Lokondera

Masiku ano, mayiko ambiri n’ngolemera komano anthu ambirimbiri ali paumphawi wadzaoneni. Kodi anthu osauka angayembekezere kusintha kulikonse?

3 Kodi Ndani Akudyerera Chuma cha Dzikoli?

4 N’chifukwa Chiyani Ambiri Ali Osauka M’dziko Lolemerali?

7 Kodi Osauka Angayembekezere Zotani?

11 Zochitika Padzikoli

14 Adziweni Anthu a ku East Timor

20 Sindinenso Kapolo wa Mowa

23 “Mbalame ya Chinsansa” mu ngalande za ku Venice

26 Kodi Mungadye Mbozi?

28 N’chifukwa Chiyani Muyenera Kumakaonana ndi Dokotala wa Mano?

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Kodi Ndani Ali Otsatira Oona a Khristu?

Kodi Mulungu Analemberatu Tsogolo Lanu? 12

Kodi Mulungu anakonzeratu kapena kulemberatu mapeto a zochita zanu zonse ndiponso nthawi yeniyeni imene mudzafe?

Kodi Munthu Ameneyu Ndi Woyenera Kumanga Naye Banja? 18

Kodi mungadziwe bwanji kuti munthu amene muli naye pachibwenzi n’ngoyenerera kumanga naye banja?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena