Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 8/10 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2010
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mumawadziwa Anthu Otchedwa a Batak?
    Galamukani!—2010
  • Mapiko a Tombolombo
    Galamukani!—2010
  • Mahatchi Ofatsa Koma Amphamvu
    Galamukani!—2010
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2010
Onani Zambiri
Galamukani!—2010
g 8/10 tsamba 1-2

Zamkatimu

August 2010

Kodi Mumadziwa Zotani Zokhudza Mboni za Yehova?

Kodi mwamvapo zotani zokhudza Mboni za Yehova? Kodi zimene munamvazo n’zoona? Tikukhulupirira kuti nkhanizi zikuthandizani kudziwa zoona zenizeni.

3 Kodi Mumadziwa Zotani Zokhudza Mboni za Yehova?

4 Zimene Ena Amanena

6 Mafunso Amene Anthu Amakonda Kufunsa

8 Kodi Mboni za Yehova Zimakhulupirira Chiyani?

10 Loya Amene Anafufuza Zimene Mboni za Yehova Zimaphunzitsa

20 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Ziwanda N’zotani?

22 Ndikungoona Kuchedwa Kuti Ndidzawauze Kuti, “Tonse Tilipo”

24 Mahatchi Ofatsa Koma Amphamvu

25 Panagona Luso!

Mapiko a Tombolombo

26 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwirizana ndi Abale Anga?

30 Zochitika Padzikoli

31 Zoti Banja Likambirane

32 Kodi Mboni za Yehova Zimaphunzitsa Bwanji Baibulo?

Matenda Otupa Chiwindi Amapha Mwakabisira 12

Pafupifupi munthu mmodzi pa anthu atatu alionse padziko lonse ali ndi matenda amenewa. Matendawa ndi oopsa kwambiri ndipo amapha. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe mmene mungadzitetezere.

Kodi Mumawadziwa Anthu Otchedwa a Batak? 16

Ku Indonesia kuli anthu ambiri a mtundu wa Batak ndipo chiwerengero chawo chimaposa mitundu ina yonse ya m’dzikoli. Dera limene anthuwa amakhala ndi lokongola kwambiri ndipo nyengo yake ndi yabwino. Werengani nkhaniyi kuti muphunzire zambiri zokhudza chikhalidwe cha anthu amenewa.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

© Sebastian Kaulitzki/Alamy

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena