Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 1/13 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
Onani Zambiri
Galamukani!—2013
g 1/13 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

NKHANI ZOYAMBILIRA: Mmene Mungalerere Ana Anu Kuti Asakhale Odzikonda Tsamba 8 Mpaka 11

3 Zochitika Padzikoli

4 Mfundo Zothandiza Mabanja

Zimene Mungachite Kuti Muzimasukirana ndi Mwana Wanu

6 Kucheza ndi Anthu

Wasayansi Akufotokoza za Chikhulupiriro Chake

12 Anthu ndi Mayiko

Dziko la Cameroon

14 Zimene Baibulo Limanena

Paradaiso

16 Kodi Zinangochitika Zokha?

Mbalame Yotha Kuuluka Ulendo Wautali

MUNGAPEZE ZAMBIRI PA WEBUSAITI YA

www.jw.org

ACHINYAMATA

ZIMENE ACHINYAMATA AMADZIFUNSA

Kodi Ndizitani Ngati Ena Akundichitira Zachipongwe?

Mtsikana wina, dzina lake Coretta ananena kuti: “Ku sukulu kwathu, anyamata ankandikoka khamisolo, n’kumandiuza zinthu zopusa ngati mmene ndingasangalalire nditati ndagona nawo.” Kodi mukanakhala inuyo mukanatani? Anthu akhoza kusiya kukuchitirani zachipongwe ngati mutadziwa zoyenera kuchita ngati anthu akukuchitirani zachipongwe.

ANA

ZITHUNZI

Chitani dawunilodi ndi kupulinta chithunzi. Kenako malizitsani chithunzicho limodzi ndi ana anu. Athandizeni kudziwa zambiri za anthu a m’Baibulo komanso kuphunzira makhalidwe abwino.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena