Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 4/13 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2014
Onani Zambiri
Galamukani!—2013
g 4/13 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

NKHANI YA PACHIKUTO N’zotheka Kuthetsa Nkhanza za M’banja Tsamba 8 Mpaka 11

3 Zochitika Padzikoli

4 Mfundo Zothandiza Mabanja

Kodi Mungapewe Bwanji Kulankhula Mawu Achipongwe?

6 Kucheza ndi Anthu

“Sindimakayikiranso Zoti Mulungu Analenga Zamoyo Zonse”

12 Anthu ndi Mayiko

Dziko la Indonesia

14 Zimene Baibulo Limanena

Thanzi Lathu

16 Mukhoza Kulowa pa Webusaiti Yathu Mosavuta

MUNGAPEZE ZAMBIRI PA WEBUSAITI YA

www.jw.org

ACHINYAMATA

ZIMENE ACHINYAMATA AMADZIFUNSA

Kodi Ndingatani Ngati Anzanga Amandivutitsa Kusukulu?

Mtsikana wina yemwe ali ndi zaka 20, dzina lake Celine, ananena kuti: “Sindidzaiwala mayina amene anzanga ankandipatsa komanso mawu amwano omwe ankandinena kusukulu. Zomwe ankandinenazo zinkandipangitsa kudziona kuti ndine munthu wachabechabe, wosafunika komanso wopanda nzeru. Ndimaona kuti zikanakhala bwino akanamandimenya kusiyana n’kundinena mawu achipongwewo.” Nkhani ya pa Intaneti imeneyi ikuyankha mafunso monga akuti: N’chifukwa chiyani ana ena amakonda kuvutitsa anzawo? Ndani amene nthawi zambiri amavutitsidwa? Kodi mungatani ngati anzanu amakuvutitsani?

(Fufuzani pa mawu akuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA/ACHINYAMATA)

ANA

Werengani nkhani zomwe zafotokozedwa pogwiritsa ntchito zithunzi. Gwiritsani ntchito nkhanizi kuthandizira ana anu kudziwa zambiri za anthu otchulidwa m’Baibulo komanso kuwathandiza kuti akhale ndi makhalidwe abwino.

(Fufuzani pa mawu akuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA/ANA)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena