Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 3/14 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2014
  • Nkhani Yofanana
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2014
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2014
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2014
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2014
Onani Zambiri
Galamukani!—2014
g 3/14 tsamba 1-2

Zamkatimu

March 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.

NKHANI YA PACHIKUTO

Kodi Mukudziwa Mmene Mulungu Analengera Zinthu Zonsezi?

TSAMBA 4 MPAKA 7

3 Zochitika Padzikoli

8 Zimene Baibulo Limanena

Ndalama

10 Anthu ndi Mayiko

Dziko la El Salvador

12 Misozi Yathu Ndi Yodabwitsa Kwambiri

14 Mfundo Zothandiza Mabanja

Ngati Banja Lanu Silikuyenda Bwino

16 Kodi Zinangochitika Zokha?

Khungu la Njoka

MUNGAWERENGENSO NKHANI ZOTSATIRAZI PA WEBUSAITI YA

www.pr418.com

ACHINYAMATA

Mungapeze mayankho ochokera m’Baibulo a mafunso ambiri amene achinyamata amakhala nawo. Nkhani zake ndi monga:

• “Kodi Ndingatani Ngati Palibe Munthu Amene Ndingacheze Naye Momasuka?”

• “Kodi Ndingatani Kuti Ndisamachite Zinthu Mozengereza?”

• “Kodi Munthu Ameneyu Ndi Woyenera Kuti Ndimange Naye Banja?”

(Fufuzani pa mawu akuti, ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA)

ANA

Werengani nkhani zomwe zafotokozedwa pogwiritsa ntchito zithunzi. Gwiritsani ntchito nkhanizi kuthandiza ana anu kudziwa zambiri za anthu otchulidwa m’Baibulo komanso kuwathandiza kuti akhale ndi makhalidwe abwino.

(Fufuzani pa mawu akuti, ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ANA)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena