Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g20 No. 2 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Galamukani!—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mungatani Mutakumana Ndi Vuto Lalikulu?
    Galamukani!—2014
  • Kodi Tsogolo Lathu Linalembedweratu?
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Kodi Muyenera Kukhulupirira Kuti Munthu Akafa Amabadwanso m’Moyo Wina?
    Nsanja ya Olonda—1997
  • N’chifukwa Chiyani Anthu Abwino Nawonso Amakumana Ndi Mavuto?
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Galamukani!—2020
g20 No. 2 tsamba 2
Chipinda chodikirira cha ku chipatala. Dokotala akupereka uthenga wachisoni kwa banja lina lomwe laimirira pafupi ndi khomo lolowera. Anthu ena akudikirira kuti aonane ndi adokotala.

Mawu Oyamba

Nthawi zina tonsefe timakumana ndi mavuto monga matenda, ngozi zam’chilengedwe ndiponso ngozi zina, kapena zachiwawa.

Anthu akufufuza mayankho.

  • Anthu ena amanena kuti timavutika chifukwa chakuti Mulungu analemberatu kuti tidzakumana ndi mavuto, kapena amati palibe zambiri zomwe tingachite kuti tisamavutike.

  • Ena amati timavutika chifukwa cha zinthu zoipa zomwe tinachita m’mbuyomu kapena m’moyo wina womwe tinali nawo tisanabadwe m’moyo uno.

Mavuto amachititsa anthu kukhala ndi mafunso ambiri opanda mayankho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena