Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Lmn tsamba 31
  • ‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’
  • “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’
    “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Mungapeze buku lina
    Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
  • Mabuku Ogawira
    Kupulumuka Kuloŵa m’Dziko Lapansi Latsopano
  • Timoteo—‘Mwana Weniweni m’Chikhulupiriro’
    Nsanja ya Olonda—1999
Onani Zambiri
“Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
Lmn tsamba 31

‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’

Izi n’zimene mtumwi Paulo analembera mnyamatayo Timoteo. (2 Timoteo 3:14) Popeza kuti mwawerenga bukuli, mwadziwa zinthu zabwino zambiri zimene Mulungu wasungira anthu amene amam’konda. Koma mufunikabe kupita patsogolo mwauzimu. Mboni za Yehova n’zokonzeka kukuthandizani ngati palibe wina amene akukuthandizani. Tangolemberani Mboni za Yehova kugwiritsa ntchito imodzi ya maadiresi ali pansipa, ngati mukufuna kudziwa zambiri kapena ngati mukufuna kuti wa Mboni za Yehova azibwera kunyumba kwanu kudzaphunzira nanu Baibulo nthawi zonse kwaulere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena