Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • su tsamba 191
  • Mabuku Ogawira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mabuku Ogawira
  • Kupulumuka Kuloŵa m’Dziko Lapansi Latsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Mungapeze buku lina
    Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
  • “Pitiriza m’Zinthu Zimene Unaphunzira”
    Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • ‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’
    “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Kodi ndi Buku la Inunso?
    Buku la Anthu Onse
Onani Zambiri
Kupulumuka Kuloŵa m’Dziko Lapansi Latsopano
su tsamba 191

Mabuku Ogawira

KONZEKERANI TSOPANO KUKHALA M’DZIKO LAPANSI LATSOPANO LA MULUNGU

Gulani ndi kuŵerenga—

MUNGATHE KUKHALA NDI MOYO KOSATHA M’PARADAISO PA DZIKO LAPANSI

Limaphatikizapo mayankho okhutiritsa maganizo Abaibulo a mafunso onga ngati:

● Kodi chimachitika nchiyani pa imfa?

● Kodi nchifukwa ninji Mulungu walola kuipa?

● Kodi ndimotani mmene Baibulo lingakuthandizireni kukhala ndi moyo wabanja wachimwemwe?

Limagogomezera chiyembekezo cha moyo wamuyaya m’Paradaiso wa padziko lapansi.

Lazithunzithunzi zokongola; losavuta kumva; lamasamba 256.

OGWIRIZANA M’KULAMBIRIDWA KWA MULUNGU YEKHA WOWONA

Lolinganizidwa kukulitsa ndi kuzamitsa chidziŵitso chanu cha Mawu a Mulungu.

Limakuthandizani kuphunzira mmene mungagwiritsirire ntchito ziphunzitso Zabaibulo mokwanira kwambiri m’moyo wanu.

Laling’ono; lamasamba 192.

AŴIRIŴA AMACHITA $5,60 ZOKHA.

Tumizani oda yanu ku Watch Tower, mukumagwiritsira ntchito keyala yapafupi koposa ya osonyezedwa patsamba lotsatira. Mitengo njokhoza kusintha.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena