Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • pe tsamba 256
  • “Pitiriza m’Zinthu Zimene Unaphunzira”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Pitiriza m’Zinthu Zimene Unaphunzira”
  • Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’
    “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Mungapeze buku lina
    Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
  • Mabuku Ogawira
    Kupulumuka Kuloŵa m’Dziko Lapansi Latsopano
  • Timoteo—‘Mwana Weniweni m’Chikhulupiriro’
    Nsanja ya Olonda—1999
Onani Zambiri
Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
pe tsamba 256

“Pitiriza m’Zinthu Zimene Unaphunzira”

Zimenezo ndizo zimene Mtumwi Paulo analembera Timoteo wachichepereyo. (2 Timoteo 3:14, NW) Pambuyo pa kuwerenga bukhu lino, mukudziwa zinthu zabwino zambiri zimene Mulungu wasungira awo amene akumkonda. Koma mufunikira kupitiriza kupita patsogolo m’njira yauzimu. Mboni za Yehova zidzakhala zokondwa kukuthandizani, ngati inu simuli kale kulandira chithandizo chimenecho. Ingolemberani kalata ku Watch Tower ku keyala yoyenerera, monga momwe andandalikidwira pansipa, mukumapempha chidziwitso chowonjezereka kapena kuti mmodzi wa Mboni za Yehova adze kunyumba kwanu ndi kuphunzira nanu Baibulo nthawi zonse popanda malipiro.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena