Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • tp tsamba 188
  • Mungapeze buku lina

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mungapeze buku lina
  • Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • Mabuku Ogawira
    Kupulumuka Kuloŵa m’Dziko Lapansi Latsopano
  • “Pitiriza m’Zinthu Zimene Unaphunzira”
    Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • ‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’
    “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Kodi ndi Buku la Inunso?
    Buku la Anthu Onse
Onani Zambiri
Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
tp tsamba 188

Mungapeze buku lina

Nkhani Zabaibulo Zokondweretsa Ana

Kuyambira pakutulutsidwa kwake, Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo lakhala lokondweretsa achichepere ndi achikulire omwe. Achichepere amakondwera kuti nkhani 116 ziŵerengedwe kwa iwo mobwerezabwereza. Bukhuli liri ndi masamba 256, lachikuto chagolidi yachikasu limodzi ndi dzina m’zilembo zofiira, ndi zazikulu kwambiri. Liri ndi zithunzithunzi zazikulu zoposa 125 zimene unyinji wake ziri zamawonekedwe amitundu ingapo. Limachita $4,00 zokha, zopositira zaphatikizidwa. (Chiŵerengerochi chingathe kusintha.) Lemberani ku Watch Tower, mukumagwiritsira ntchito keyala kuchokera ku chikuto chakumbuyo.

Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi

Bukhu limeneli limafola chowonadi chamaziko cha Baibulo ndipo limagogomezera chiyembekezo cha moyo wamuyaya m’paradaiso padziko lapansi. Limaphatikizapo mafunso onga akuti: Kodi chimachitika nchiyani pa imfa? Chiukiriro—cha ayani ndipo kuti? Kodi nchifukwa ninji Mulungu walola kuipa? Kodi Baibulo lingakuthandizeni motani kuti mukhale ndi moyo wa banja wachimwemwe? Lomveka mosavuta. Lazithunzithunzi zokongola, lamasamba akuru, 256. Lopezeka pa chopereka cha $4,00 (Zimbabwe). (Chiŵerengerochi chingathe kusintha.) Lemberani ku Watch Tower, mukumagwiritsira ntchito keyala kuchokera pa tsamba lomalizira.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena