Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp20 No. 1 tsamba 16
  • Mmene Kudziwa Choonadi Kungakuthandizireni

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mmene Kudziwa Choonadi Kungakuthandizireni
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2020
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • KODI MUYENERA KUCHITA CHIYANI?
  • “Amakuderani Nkhawa”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2019
  • Kodi Munayamba Mwadzifunsapo Kuti:
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2020
  • Mungathe Kukhala pa Ubwenzi ndi Mulungu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2019
  • Kodi Mukuganiza Kuti Zinthu Zidzakhala Bwanji M’tsogolo?
    Kodi Mukuganiza Kuti Zinthu Zidzakhala Bwanji M’tsogolo?
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2020
wp20 No. 1 tsamba 16

Mmene Kudziwa Choonadi Kungakuthandizireni

Mulungu, amene nthawi zonse amanena zoona, akukupatsani mwayi woti mukhale ndi chiyembekezo cha “moyo wosatha.”​—Yohane 3:16.

KODI MUYENERA KUCHITA CHIYANI?

Mtsikana akuwerenga Baibulo patabuleti
  • Phunzirani zimene Mawu a Mulungu omwe ndi choonadi amanena.—Yohane 17:3, 17.

  • Sankhani kumvera Mulungu.—Deuteronomo 30:19, 20.

  • Muzitsatira malangizo a Mulungu, omwe ndi othandiza.​—Yakobo 1:25.

A Mboni za Yehova padziko lonse lapansi akupindula chifukwa chophunzira choonadi cha m’Baibulo. Iwo ndi okonzeka kukuuzani zimene amaphunzirazo.

Kuti mudziwe zambiri, onani kabuku kakuti, Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale. Kabukuka ndi kofalitsidwa ndi Mboni za Yehova ndipo kakupezekanso pa www.jw.org/ny.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena