Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/03 tsamba 3
  • Mmene Mungafalitsire Buku la Yandikirani kwa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mmene Mungafalitsire Buku la Yandikirani kwa Yehova
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Maulaliki a Utumiki wa Kumunda
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Pindulani Pophunzira Buku la Yandikirani kwa Yehova
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2004
  • Kodi Mulungu Ndani?
    Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
km 1/03 tsamba 3

Mmene Mungafalitsire Buku la Yandikirani kwa Yehova

◼ Baibulo lanu lili kumanja, nenani kuti: “Anthu ambiri okhulupirira Mulungu amafuna kuyandikana naye kwambiri. Kodi mumadziŵa kuti Mulungu amatipempha kuyandikira kwa iye? [Ŵerengani Yakobo 4:8.] Buku ili lakonzedwa kuti litithandize kuyandikira kwa Mulungu pogwiritsira ntchito Baibulo lathulathu.” Ŵerengani ndime 1 patsamba 16.

◼ Baibulo lanu lili kumanja, nenani kuti: “Lerolino, m’dziko muli kupanda chilungamo. Zinthu zili mmene afotokozera apa. [Ŵerengani Mlaliki 8:9b.] Ena amadabwa ngati Mulungu zimam’khudza n’komwe. [Ŵerengani ziganizo ziŵiri zoyambirira m’ndime 4 patsamba 119.] Mutu umenewu ukufotokoza chifukwa chake Mulungu walola kupanda chilungamo kwakanthaŵi.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena