Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/03 tsamba 4
  • Zinthu Zotithandiza Kuti Tipeŵe Magazi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zinthu Zotithandiza Kuti Tipeŵe Magazi
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikonzekereratu Panopa Zimene Mudzachite Mukadzadwala
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Makhadi a Ngongole Kodi Adzakutumikirani Kapena Kukupangani Kapolo?
    Galamukani!—1997
  • Kodi Mumanyalanyaza?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Kodi Mukugwiritsa Ntchito Bwino Makadi Odziwitsa Anthu za JW.ORG?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
km 12/03 tsamba 4

Zinthu Zotithandiza Kuti Tipeŵe Magazi

Ofalitsa obatizidwa omwe m’mbuyomu analemba khadi la Chidziŵitso kwa Madokotala/Chowamasula ku Mlandu kapena Khadi la Mwana afunika kulemba makadi atsopano chaka chino. Pa Msonkhano wa Utumiki wa mlungu woyambira December 29, mlembi akhale ndi makadi okwanira ofalitsa obatizidwa ndi ana awo. Ngati mpingo ulibe makadi okwanira, mlembi angafufuze ku mipingo yomwe wayandikana nayo kapena aitanitse makadi ena mpingo ukamaitanitsa mabuku paulendo wotsatira.

Makadiŵa akalembedwere kunyumba bwinobwino koma OSASAINA. Makadiŵa adzasainidwe, kuchitira umboni, ndiponso kulemba deti pa Phunziro la Buku la Mpingo lotsatira, ndipo woyang’anira phunziro la bukulo angathandize amene akufuna thandizo. Anthu ochitira umboni afunika kuona mwini khadilo akulisaina.

Ofalitsa osabatizidwa angadzilembere makadi awo ndiponso a ana awo mwa kukopera zomwe zili pa khadi la Chidziŵitso kwa Madokotala/Chowamasula ku Mlandu ndi pa Khadi la Mwana.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena