Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/15 tsamba 4
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Zomwe Munganene Pogaŵira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 4/15 tsamba 4

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda May 1

“Mutakhala ndi mphamvu zothetsa mavuto, kodi ndi vuto liti lomwe mungathetse? [Yembekezerani ayankhe.] Baibulo limanena kuti posachedwapa Mulungu athetsa vuto limeneli komanso ena onse. [Werengani lemba logwirizana ndi zimene wayankhazo. Malemba ake ndi monga, Danieli 2:44; Miyambo 2:21, 22; Mateyu 7:21-23 kapena 2 Petulo 3:7.] Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza kuti Mulungu adzachita zimenezi posachedwapa. Yafotokozanso mmene adzachitire zimenezi.”

Galamukani! May

“Kodi mukuganiza kuti zingatheke kuti umphawi uthe komanso kuti aliyense akhale ndi nyumba yabwino? [Yembekezerani ayankhe.] Taonani zimene Mulungu walonjeza pa nkhaniyi. [Werengani Yesaya 65:21-22.] Galamukani! iyi ikufotokoza mmene Mulungu adzachitire zimenezi komanso zimene tingachite kuti tidzakhalepo pa nthawiyi.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena