Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • GALAMUKANI!
  • GALAMUKANI!
  • MVERANI MULUNGU KUTI MUDZAPEZE MOYO WOSATHA
  • LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 August tsamba 1
Akulalikira pogwiritsa ntchito intakomu ku Vienna, m’dziko la Austria

Akulalikira pogwiritsa ntchito intakomu ku Vienna, m’dziko la Austria

Zitsanzo za Ulaliki

GALAMUKANI!

Galamukani! Na. 4 | Kodi N’zotheka Kusintha Zomwe Munazolowera?

Funso: Kodi mukuganiza kuti zinthu zingakhale bwino padzikoli ngati anthu onse atasiya zoipa zimene anazolowera kuchita n’kumayesetsa kuchita zabwino?

Lemba: Mlal. 7:8a

Perekani Magaziniyo: Nkhani za m’magaziniyi zikufotokoza mfundo za m’Baibulo zomwe zingathandize anthu kuti azikonda kuchita zinthu zabwino.

GALAMUKANI!

Funso: Nthawi zina zinthu zingasinthe mosayembekezereka pa moyo wathu ndipo palibe zomwe tingachite kuti zimenezi zisachitike. Kodi mukuganiza kuti munthu angatani ngati zinthu zasintha pa moyo wake?

Lemba: Mlal. 7:10

Perekani magaziniyo: [Musonyezeni nkhani imene ikuyambira patsamba 10.] Nkhaniyi ikufotokoza mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize zinthu zikasintha pa moyo wathu.

MVERANI MULUNGU KUTI MUDZAPEZE MOYO WOSATHA

Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha

Funso: Aliyense, kuphatikizapo achibale komanso anzathu, ali ndi dzina. Koma nanga bwanji Mulungu, kodi nayenso ali ndi dzina? Nanga dzina lake ndi ndani?

Lemba: Sal. 83:18

Perekani Kabukuko: Kabuku aka kakufotokoza zinthu zinanso zomwe Baibulo limanena zokhudza Mulungu. [Musonyezeni tsamba 6 ndi 7.]

LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena