Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsamba 4
  • Mukhoza Kumachitabe Zambiri Ngakhale Muli Okalamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mukhoza Kumachitabe Zambiri Ngakhale Muli Okalamba
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Okalamba ndi Ofunika Kwambiri pa Ubale Wathu Wachikristu
    Nsanja ya Olonda—2004
  • “Mubale Chipatso Chambiri”
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Ananu, Kodi Mukuyesetsa Kuti Yehova Akhale Mnzanu Wapamtima?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Yehova Amakonda Anthu Amene ‘Amabereka Zipatso’ Mopirira
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 August tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 92-101

Mukhoza Kumachitabe Zambiri Ngakhale Muli Okalamba

Munthu wachikulire akuyenda ndi wachinyamata pafupi ndi mtengo wa kanjedza

92:12

Mtengo wa kanjedza umatha kukhala zaka zoposa 100 koma n’kumaberekabe zipatso. Nawonso achikulire akhoza kumachitabe zambiri mofanana ndi mtengo umenewu

Achikulire akhoza kumachita zotsatirazi:

92:13-15

  • Kupempherera ena

  • Kuphunzira Baibulo

  • Kusonkhana komanso kupereka ndemanga

  • Kuuza ena zomwe zinawachikira pa moyo wawo

  • Kulalikira ndi mtima wonse

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena