Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 June tsamba 5
  • Ananu, Kodi Mukuyesetsa Kuti Yehova Akhale Mnzanu Wapamtima?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ananu, Kodi Mukuyesetsa Kuti Yehova Akhale Mnzanu Wapamtima?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ndinu Munthu Wakuthupi Kapena Munthu Wauzimu?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Tili ndi Chuma Chamtengo Wapatali Chofunika Kugawira Ena
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2008
  • Yesetsani Kuti Mukhale Oyang’anira
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Kuthandiza Mwana Kuti Akule mu Nzeru ya Umulungu
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 June tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LUKA 2-3

Ananu, Kodi Mukuyesetsa Kuti Yehova Akhale Mnzanu Wapamtima?

Kuyambira ali mwana, Yesu anapereka chitsanzo chabwino pa nkhani yochita zimene Yehova amafuna komanso kulemekeza makolo ake.

Ananu, kodi mungatsanzire bwanji Yesu m’njira zotsatirazi?

  • 2:41, 42

    Yesu akupita ku Yerusalemu kukachita Pasika limodzi ndi banja lakwawo

    Kuchita zinthu zokhudza kulambira:

  • 2:46, 47

    Yesu ali ndi zaka 12 ndipo ali limodzi ndi aphunzitsi kukachisi

    Kumvetsa bwino Malemba:

  • 2:51, 52

    Yesu akumvera makolo ake

    Kulemekeza makolo anu:

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena